by Admin | Nov 9, 2018 | Salaat
Kukhala pa Mpando Poswali (Munthu yemwe akuloledwa kuswaali atakhala pampando akhale otani) 1. Akhale kuti akulephera kuimilira pa Swalaat Kuphatikiza kulephera kupanga rukuu’ ndi sajda molongosoka. Choncho aswali chokhala. Monga mmene Mtumiki salla Allah alaih...
Your Comments