by Admin | Dec 23, 2018 | Misconceptions
Salaf ndi liwu lomwe limatanthauza zinthu zomwe zidapita, za mbuyomu. Ndipo liwuli likamagwiritsidwa ntchito mchipembedzo cha Chisilamu limatanthauza mibadwo ya anthu akale omwe anayambilira kugwiritsa ntchito Shariah. Tsopano mibadwo imeneyi kuyambira pa...
Your Comments