by Admin | Jun 28, 2019 | Prophets
Pambuyo pa chigumula, anthu a Nuh alaih salaam anachulukana padziko. Mneneri Nuh alaih salaam anali ndi ana komanso zidzulu zambiri, choncho chiwelengero cha anthu padziko chinakula. Ambiri mwa iwo anakhanzikika ku Yemen. Zimakambidwa kuti omwe anakhanzikika kumeneko...
Your Comments