by Admin | Jul 26, 2020 | Featured, Hajj
Pangani Download ma Khutbah a Eidul Adh’ha (PDF) خطبة عيد الأضحى المبارك خطبة عيد الأضحى المبارك اخطبة عيد الأضحى...
by Admin | Jul 26, 2020 | Fatawa, Featured, Islam
Mafunso omwe timafunsa pa za deen timafuna kudziwa kuti kodi deen yathu tiyendetse bwanji. Timafuna kudziwa kuti kodi ibaada tingachite bwanji, nanga chikhulupiliro chathu tingachisamale bwanji. Kudzera mu kufuna kudziwa zinthu momwemo, ambiri tili ndi chizolowezi...
by Admin | Jul 19, 2020 | Featured, Islam
Ndimafunsidwa kawirikawiri: “…ndinu wa Sunni … Qadriyya … Shia … Ashaaira … kapena Muutazila?? Koma ine mainawa ndimangomva sindikudziwa kuti ndichani. Ndiye ndimafuna ntadziwa kuti zikutanthauza chani, komanso ndikufunikira kwanji...
by Admin | Jul 19, 2020 | Featured, Fiqh
Swalat ya Jum’ah simaswalidwa ngati anthu sanakwane jamaah (gulu). Koma ma chicfukwa cha kusapezeka umboni wochokera kwa Mtumiki salla Allah alaih wasallam osonyeza chiwelegero chenicheni cha anthu omwe akukwanira kupanga jamaah, ma ulamaa pambuyo popanga...
by Admin | Jul 19, 2020 | Featured, Islam
Msilamu asamalimbane ndi kutsatira maina, magulu kapena zirizonse zomwe zikuonetsa kugawika kwa Ummah. Koma ndizofunika kwa iye kuzidziwa munjira ya kuphunzira, akadziphunzira afalitse choona chenicheni chomwe Asilamu atsatire. Imeneyo ndiye Da’wah ya Sheikh...
by Admin | Jul 18, 2020 | Featured, Islam
Nkhani ya zithunzi ndi yaitali chifukwa imakhudza mbali zambiri zomwe zimakhala zosiyana zigamulo zake, monga kukhala zoletsedwa kapena zololedwa kapena kuletsedwa kotheratu, mopanda kupatula komanso kuletsedwa kopatula. Pali ma aayah a mu Qur’an komanso...
Your Comments