Chuma cha Mkazi

Zipembedzo zitatuzi zili ndi chikhulupiliro chosagwedezeka pa kufunikira kwa ukwati ndi banja. Ndipo zimavomerezana pa utsogoleri wa mwamuna pa banja. Komabe, pali kusiyana kwakukulu pakati pa zipembedzozi, pa malire a utsogoleri umenewu. Chikhalidwe cha Chiyuda ndi...

Malumbiro

Malingana ndi Baibulo, munthu ayenera kukwaniritsa malonjezo omwe angapange kwa Mulungu. Iye sayenera kutswa liwu lake. Koma lumbiro la mkazi silikhala lokakamizidwa pa iye; iye akuyenera kuloledwa ndi bambo ake, ngati ali osakwatiwa; kapena ndi mwamuna wake, ngati...

Chiwerewere

Chiwerewere ndi tchimo muzipembedzo zonse. Baibulo linaika chilango cha imfa kwa wachiwerewere wamwamuna ndi wamkazi (Levitiko 20:10). Chisilamu chimalanganso chimodzimodzi wachiwerewere wa mwamuna ndi wamkazi (24: 2). Komatu ngakhale zili choncho, tanthauzo la...

Kuikira Umboni kwa Mkazi

Nkhani ina yomwe Qur’an ndi Baibulo sizimagwirizana ndi ya mkazi yemwe akuikira umboni. Ndi zowona kuti Qur’an inalangiza okhulupilira omwe akugwirizana ngongole ya chuma kuti apeze mboni ziwiri zazimuna kapena mwamuna mmodzi ndi akazi awiri (2:282). Ndi...

Kodi Mkazi Ndi Wodetsedwa?

Malamulo a Chiyuda okhunzana ndi mkazi yemwe akusamba, ndi ovuta kwambiri kuwamvetsa. Chipangano Chakale chimaona kuti mkazi yemwe akusamba ndi wodetsedwa, komanso kudetsedwa kwake “kumapangitsa ena kuti akhale odetsedwa (opanda twahara)”. Aliyense kapena...

Maphunziro a Ana Achikazi

Kusiyana kwa pakati pa Baibulo ndi  Qur’an pa malamulo okhunza mkazi, kulibe malire pa ana achikazi ongobadwa kumene, iwo akusiyanabe kwambiri. Tiyeni tifananitse Baibulo ndi Qur’an pa mwana wamkazi yemwe akufuna kuyamba kuphunzira: Tsinde la Chiyuda ndi...