by Admin | Jul 27, 2020 | Featured, Islam
عن عائشة رضي الله عنها قالت: قلت: يا رسول الله، ابن جُدعانَ كان في الجاهلية يصل الرحم ويطعم المسكين، فهل ذاك نافع؟ قال: لا ينفعه، إنه لم يقل يوما: رب اغفرلي خطيئتي يوم الدين Aisha radhia Allah anha anati: Ee Mtumiki wa Allah, mwana wa Jud’aan munthawi yaumbuli...
by Admin | Jul 26, 2020 | Featured, Hajj
Pangani Download ma Khutbah a Eidul Adh’ha (PDF) خطبة عيد الأضحى المبارك خطبة عيد الأضحى المبارك اخطبة عيد الأضحى...
by Admin | Jul 26, 2020 | Fatawa, Featured, Islam
Mafunso omwe timafunsa pa za deen timafuna kudziwa kuti kodi deen yathu tiyendetse bwanji. Timafuna kudziwa kuti kodi ibaada tingachite bwanji, nanga chikhulupiliro chathu tingachisamale bwanji. Kudzera mu kufuna kudziwa zinthu momwemo, ambiri tili ndi chizolowezi...
by Admin | Jul 19, 2020 | Featured, Islam
Ndimafunsidwa kawirikawiri: “…ndinu wa Sunni … Qadriyya … Shia … Ashaaira … kapena Muutazila?? Koma ine mainawa ndimangomva sindikudziwa kuti ndichani. Ndiye ndimafuna ntadziwa kuti zikutanthauza chani, komanso ndikufunikira kwanji...
by Admin | Jul 19, 2020 | Featured, Fiqh
Swalat ya Jum’ah simaswalidwa ngati anthu sanakwane jamaah (gulu). Koma ma chicfukwa cha kusapezeka umboni wochokera kwa Mtumiki salla Allah alaih wasallam osonyeza chiwelegero chenicheni cha anthu omwe akukwanira kupanga jamaah, ma ulamaa pambuyo popanga...
Your Comments