Learn Islam

0x1c8c5b6a

0x1c8c5b6a

PKV QQ Online: Pilihan Tepat Bermain BadarQQ di Situs Terpercaya Server MataQQ 365

Di tengah maraknya permainan judi online, PKV QQ Online menjadi salah satu platform yang paling diminati oleh para pecinta game kartu. Salah satu varian game yang tak kalah populer adalah BadarQQ Online, yang kini dapat dimainkan secara nyaman dan aman di situs...

Kwa Omwe Amanyoza Mai Wathu Aaisha radhia Allahu anha

Ma Shia amamunena Mai wathu Wolemekezeka Aisha radhia Allahu anha kuti ndi munaafiq, komanso ndi wachimasomaso. Kuwonjezera pamenepo, m'mabuku mwawo akamamutchula mkazi wa Mtumiki aliyense amamutchula kuti Ummul Mu'mineena mkazi wa Mtumiki alaiha Ssalaam, pomwe Aisha...

Hudaibiya

A TURNING POINT IN THE HISTORY OF ISLAM. Abdulkarim Shuaib May 20, 2022 02:56AM (Source: Book of Seerah ibn Hisham and Arab news 2012 religion article) The incident of Hudaibiyah reserves in history a significant phase of Islam when Muslims got an opportunity to...

Chisangalalo cha Nikaah pa Shari’ah

Tisaiwale kukumbukira kuti Kusangalala tsiku la Nikkah, sikuti Ndi chikakamizo ayi, koma kuti ndi Sunnah, chifukwa Anthu amazikakamiza ndikupanikizika Poona kuti afune asafune akuyenera kuchititsa Chisangalalo cha Nikkah yawo,dziwani kuti Kumangitsa Nikkah ndi chinthu...

Lamulo la Kusunga Katundu Nkudzagulitsa Munyengo Yokwera Mtengo

Pakukhala kuti Chisilamu chidaunikira mbali zonse za umoyo, Mu Qur'an ndi Mahadith (zoyankhula za mtumiki). Ndipo masahabah Adagwira ntchito yotamandika yotulutsa khokwe za maphunziro kuchokera mu Qur'an ndi Mahadith, pambuyo pawo padabweraso Ma Imam ndi anthu...

Zoyenera Kuchita pa Kutha kwa Ramadhan

Wapita mwezi wa madalitso, Mwezi wa mapemphero, mwezi wa Qur'an, mwezi opeleka Chopeleka, Mwezi ochulukitsa zabwino, wapita basi mwezi umene oluza aluza opambana apambana, apambana amene adasala mwa chikhulupiliro natsatira ziphuzitso za Sharia zakusala, apambana...

Kodi Ndiziloledwa Kumufunira Zabwino Yemwe Wamwalira sali Msilamu!

"Akalowa bwanji ku ng'anjo ya moto akadaulo, akatswiri komanso anthu ena amene anachita ndi kugwira ntchito zopambana, ndizopititsa patsogolo umoyo wa anthu pa dziko lino lapansi?. - Anthu okanira amene anagwira ntchito yotamandika pa dziko lapansi, sanagwire ntchito...

Al Bayyinah – Tiwadziwe ma Shia

Kutamandidwa konse ndi kwa Allaah, Wapamwambamwamba, Yemwe alibe wothandizana naye mu Ufumu Wake, Yemwe ali m’Modzi, Yemwe ali Wakutha kuchita chili chonse ndipo kwa Iye ndi komwe kuli Chiongoko. Mtendere ndi madalitso zipite kwa Mtumiki Muhammad (ﷺ), aku banja ake...

Zina mwa Zabodza Mmabuku a Shi’ah

Bodza la Mashia lonena kuti pali umboni woti Ali radhia Allahu anhu ndi Khalifa woyamba osati Abu Bakr radhia Allahu anhu  185- حتى لا ننخدع حقيقة الشيعة Pamene ma Swahaba wonse anagwirizana za utsogoleri komanso ulowammalo wa Abu Bakr, ‘Umar, ‘Uthman, kenako Ali...

For donations, please click below

Ngati mukufuna kuthandiza, dinani mmusimu